×

Mtundu wa anthu unali umodzi koma anasemphana pambuyo pake. Ndipo kukanapanda kuti 10:19 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yunus ⮕ (10:19) ayat 19 in Chichewa

10:19 Surah Yunus ayat 19 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yunus ayat 19 - يُونس - Page - Juz 11

﴿وَمَا كَانَ ٱلنَّاسُ إِلَّآ أُمَّةٗ وَٰحِدَةٗ فَٱخۡتَلَفُواْۚ وَلَوۡلَا كَلِمَةٞ سَبَقَتۡ مِن رَّبِّكَ لَقُضِيَ بَيۡنَهُمۡ فِيمَا فِيهِ يَخۡتَلِفُونَ ﴾
[يُونس: 19]

Mtundu wa anthu unali umodzi koma anasemphana pambuyo pake. Ndipo kukanapanda kuti Mau a Ambuye wako ananenedwa kale, mkangano wawo ukanathetsedwa

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وما كان الناس إلا أمة واحدة فاختلفوا ولولا كلمة سبقت من ربك, باللغة نيانجا

﴿وما كان الناس إلا أمة واحدة فاختلفوا ولولا كلمة سبقت من ربك﴾ [يُونس: 19]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo ndithudi anthu kalero (m’nthawi ya Adam) adali mpingo umodzi (opembedza Allah), koma adasiyana (pambuyo pake). Ndipo pakadapanda liwu lochokera kwa Mbuye wako, lomwe lidatsogola (lakuti adzawalanga tsiku la Qiyâma), ndithu kukadaweruzidwa pakati pawo m’zomwe adali kusiyana
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek