×

Kwa Iye nonse mudzabwerera. Lonjezo la Mulungu ndi loona. Iye ndiye adayamba 10:4 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yunus ⮕ (10:4) ayat 4 in Chichewa

10:4 Surah Yunus ayat 4 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yunus ayat 4 - يُونس - Page - Juz 11

﴿إِلَيۡهِ مَرۡجِعُكُمۡ جَمِيعٗاۖ وَعۡدَ ٱللَّهِ حَقًّاۚ إِنَّهُۥ يَبۡدَؤُاْ ٱلۡخَلۡقَ ثُمَّ يُعِيدُهُۥ لِيَجۡزِيَ ٱلَّذِينَ ءَامَنُواْ وَعَمِلُواْ ٱلصَّٰلِحَٰتِ بِٱلۡقِسۡطِۚ وَٱلَّذِينَ كَفَرُواْ لَهُمۡ شَرَابٞ مِّنۡ حَمِيمٖ وَعَذَابٌ أَلِيمُۢ بِمَا كَانُواْ يَكۡفُرُونَ ﴾
[يُونس: 4]

Kwa Iye nonse mudzabwerera. Lonjezo la Mulungu ndi loona. Iye ndiye adayamba kulenga zolengedwa zonse ndipo pomaliza adzazipatsanso moyo kuti adzawalipire mwa chilungamo onse amene adakhulupirira mwa Iye ndipo ankachita ntchito zabwino. Anthu osakhulupirira adzamwa zakumwa zamadzi ogaduka ndi kulandira chilango chowawa chifukwa chosakhulupirira

❮ Previous Next ❯

ترجمة: إليه مرجعكم جميعا وعد الله حقا إنه يبدأ الخلق ثم يعيده ليجزي, باللغة نيانجا

﴿إليه مرجعكم جميعا وعد الله حقا إنه يبدأ الخلق ثم يعيده ليجزي﴾ [يُونس: 4]

Khaled Ibrahim Betala
“Kobwerera kwanu nonsenu ndi kwa Iye. Ili ndilonjezo la Allah loona. Ndithu Iye ndi Yemwe adayamba kulenga (zolengedwa), ndiponso ndi Yemwe adzazibwereza (pambuyo pa imfa) kuti adzawalipire amene adakhulupirira ndi kumachita zabwino mwa chilungamo. Ndipo amene sadakhulupirire, akapeza zakumwa za madzi owira ndi chilango chopweteka chifukwa cha kusakhulupirira kwawo
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek