×

Iye ndiye amene adalipanga dzuwa kukhala muuni ndi mwezi kukhala wowala ndipo 10:5 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yunus ⮕ (10:5) ayat 5 in Chichewa

10:5 Surah Yunus ayat 5 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yunus ayat 5 - يُونس - Page - Juz 11

﴿هُوَ ٱلَّذِي جَعَلَ ٱلشَّمۡسَ ضِيَآءٗ وَٱلۡقَمَرَ نُورٗا وَقَدَّرَهُۥ مَنَازِلَ لِتَعۡلَمُواْ عَدَدَ ٱلسِّنِينَ وَٱلۡحِسَابَۚ مَا خَلَقَ ٱللَّهُ ذَٰلِكَ إِلَّا بِٱلۡحَقِّۚ يُفَصِّلُ ٱلۡأٓيَٰتِ لِقَوۡمٖ يَعۡلَمُونَ ﴾
[يُونس: 5]

Iye ndiye amene adalipanga dzuwa kukhala muuni ndi mwezi kukhala wowala ndipo adazikonzera modutsa kuti inu muzidziwa kuchuluka kwa zaka ndi chiwerengero. Iye sadazilenge chabe izo koma mu choonadi. Iye amafotokoza mawu ake momveka kwa anthu ake ozindikira

❮ Previous Next ❯

ترجمة: هو الذي جعل الشمس ضياء والقمر نورا وقدره منازل لتعلموا عدد السنين, باللغة نيانجا

﴿هو الذي جعل الشمس ضياء والقمر نورا وقدره منازل لتعلموا عدد السنين﴾ [يُونس: 5]

Khaled Ibrahim Betala
“Iye (Allah) ndiYemwe adapanga dzuwa kukhala lowala, ndi mwezi kukhala wounika; ndipo adaukonzera mbuto (masitesheni) kuti mudziwe kuchuluka kwa zaka ndi chiwerengero chake. Allah sadalenge zimenezo koma mwachoonadi (ndi cholinga cha nzeru). Akufotokoza Ayah (Zake) kwa anthu ozindikira
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek