×

Kodi anthu amene amapeka mabodza okhudza Mulungu amaganiza chiyani za tsiku la 10:60 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yunus ⮕ (10:60) ayat 60 in Chichewa

10:60 Surah Yunus ayat 60 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yunus ayat 60 - يُونس - Page - Juz 11

﴿وَمَا ظَنُّ ٱلَّذِينَ يَفۡتَرُونَ عَلَى ٱللَّهِ ٱلۡكَذِبَ يَوۡمَ ٱلۡقِيَٰمَةِۗ إِنَّ ٱللَّهَ لَذُو فَضۡلٍ عَلَى ٱلنَّاسِ وَلَٰكِنَّ أَكۡثَرَهُمۡ لَا يَشۡكُرُونَ ﴾
[يُونس: 60]

Kodi anthu amene amapeka mabodza okhudza Mulungu amaganiza chiyani za tsiku la kuuka kwa akufa? Ndithudi Mulungu ndi wabwino kwa anthu koma ambiri a iwo sathokoza ayi

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وما ظن الذين يفترون على الله الكذب يوم القيامة إن الله لذو, باللغة نيانجا

﴿وما ظن الذين يفترون على الله الكذب يوم القيامة إن الله لذو﴾ [يُونس: 60]

Khaled Ibrahim Betala
“Kodi ali ndi ganizo lotani amene akumpekera Allah bodza pa za tsiku la Qiyâma? Ndithu Allah Ndi mwini ubwino wochuluka kwa anthu. Koma ambiri a iwo sathokoza
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek