×

Mosakaika! Ndithudi Mulungu ndiye mwini wa zimene zili kumwamba ndi dziko lapansi. 10:66 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yunus ⮕ (10:66) ayat 66 in Chichewa

10:66 Surah Yunus ayat 66 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yunus ayat 66 - يُونس - Page - Juz 11

﴿أَلَآ إِنَّ لِلَّهِ مَن فِي ٱلسَّمَٰوَٰتِ وَمَن فِي ٱلۡأَرۡضِۗ وَمَا يَتَّبِعُ ٱلَّذِينَ يَدۡعُونَ مِن دُونِ ٱللَّهِ شُرَكَآءَۚ إِن يَتَّبِعُونَ إِلَّا ٱلظَّنَّ وَإِنۡ هُمۡ إِلَّا يَخۡرُصُونَ ﴾
[يُونس: 66]

Mosakaika! Ndithudi Mulungu ndiye mwini wa zimene zili kumwamba ndi dziko lapansi. Ndipo onse amene amapembedza milungu yabodza satsatira china chilichonse koma zinthu zopanda pake ndipo iwo amangopeka mabodza

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ألا إن لله من في السموات ومن في الأرض وما يتبع الذين, باللغة نيانجا

﴿ألا إن لله من في السموات ومن في الأرض وما يتبع الذين﴾ [يُونس: 66]

Khaled Ibrahim Betala
“Tamverani! Ndithu (zonse) za kumwamba ndi za pansi, nza Allah. Ndipo amene akupembedza zina kusiya Allah, satsatira aphatikizi (a Allah). Akungotsatira zoganizira, ndipo iwo sanena china koma bodza basi
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek