×

Chisangalalo cha kanthawi kochepa ka m’dziko lapansi ndipo ndi kwa Ife kumene 10:70 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yunus ⮕ (10:70) ayat 70 in Chichewa

10:70 Surah Yunus ayat 70 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yunus ayat 70 - يُونس - Page - Juz 11

﴿مَتَٰعٞ فِي ٱلدُّنۡيَا ثُمَّ إِلَيۡنَا مَرۡجِعُهُمۡ ثُمَّ نُذِيقُهُمُ ٱلۡعَذَابَ ٱلشَّدِيدَ بِمَا كَانُواْ يَكۡفُرُونَ ﴾
[يُونس: 70]

Chisangalalo cha kanthawi kochepa ka m’dziko lapansi ndipo ndi kwa Ife kumene adzabwerera ndipo Ife tidzawalawitsa chilango chowawa chifukwa cha kukana kwawo

❮ Previous Next ❯

ترجمة: متاع في الدنيا ثم إلينا مرجعهم ثم نذيقهم العذاب الشديد بما كانوا, باللغة نيانجا

﴿متاع في الدنيا ثم إلينا مرجعهم ثم نذيقهم العذاب الشديد بما كانوا﴾ [يُونس: 70]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndichisangalalo chochepa basi m’dziko lapansi. Kenako kwa Ife ndiwo mabwelero awo. Kenako tidzawalawitsa chilango chaukali chifukwa cha kusakhulupirira kwawo
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek