×

“Ndipo ngati muyamba kusakhulupirira ine sindidakupempheni mphotho. Mphotho yanga ili ndi Mulungu 10:72 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yunus ⮕ (10:72) ayat 72 in Chichewa

10:72 Surah Yunus ayat 72 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yunus ayat 72 - يُونس - Page - Juz 11

﴿فَإِن تَوَلَّيۡتُمۡ فَمَا سَأَلۡتُكُم مِّنۡ أَجۡرٍۖ إِنۡ أَجۡرِيَ إِلَّا عَلَى ٱللَّهِۖ وَأُمِرۡتُ أَنۡ أَكُونَ مِنَ ٱلۡمُسۡلِمِينَ ﴾
[يُونس: 72]

“Ndipo ngati muyamba kusakhulupirira ine sindidakupempheni mphotho. Mphotho yanga ili ndi Mulungu ndiponso ndalamulidwa kuti ndikhale mmodzi mwa ogonjera malamulo a Mulungu.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فإن توليتم فما سألتكم من أجر إن أجري إلا على الله وأمرت, باللغة نيانجا

﴿فإن توليتم فما سألتكم من أجر إن أجري إلا على الله وأمرت﴾ [يُونس: 72]

Khaled Ibrahim Betala
“Ngati mutembenuka ndikunyoza, (ndikufuna kwanu). Ine sindinakupempheni malipiro. Malipiro anga kulibe kulikonse (kumene ndingalandire) koma kwa Allah, ndipo ndalamulidwa kuti ndikhale mmodzi mwa Asilamu (ogonjera Iye).”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek