×

Ndipo pamene adaponya pansi ndodo zawo Mose adati: “Amenewa ndi matsenga ndipo 10:81 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yunus ⮕ (10:81) ayat 81 in Chichewa

10:81 Surah Yunus ayat 81 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yunus ayat 81 - يُونس - Page - Juz 11

﴿فَلَمَّآ أَلۡقَوۡاْ قَالَ مُوسَىٰ مَا جِئۡتُم بِهِ ٱلسِّحۡرُۖ إِنَّ ٱللَّهَ سَيُبۡطِلُهُۥٓ إِنَّ ٱللَّهَ لَا يُصۡلِحُ عَمَلَ ٱلۡمُفۡسِدِينَ ﴾
[يُونس: 81]

Ndipo pamene adaponya pansi ndodo zawo Mose adati: “Amenewa ndi matsenga ndipo Mulungu, ndithudi, adzagonjetsa matsenga anu. Ndithudi Mulungu savomera ntchito za anthu ochita zoipa kuti zipambane.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فلما ألقوا قال موسى ما جئتم به السحر إن الله سيبطله إن, باللغة نيانجا

﴿فلما ألقوا قال موسى ما جئتم به السحر إن الله سيبطله إن﴾ [يُونس: 81]

Khaled Ibrahim Betala
“Pamene adaponya, Mûsa adati: “Zomwe mwabweretsa ndi matsenga. Allah awaononga pompano. Ndithu Allah sakonza ntchito za oononga.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek