×

Tidavumbulutsa Mau athu kwa Mose ndi m’bale wake ponena kuti: “Amangireni nyumba 10:87 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yunus ⮕ (10:87) ayat 87 in Chichewa

10:87 Surah Yunus ayat 87 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yunus ayat 87 - يُونس - Page - Juz 11

﴿وَأَوۡحَيۡنَآ إِلَىٰ مُوسَىٰ وَأَخِيهِ أَن تَبَوَّءَا لِقَوۡمِكُمَا بِمِصۡرَ بُيُوتٗا وَٱجۡعَلُواْ بُيُوتَكُمۡ قِبۡلَةٗ وَأَقِيمُواْ ٱلصَّلَوٰةَۗ وَبَشِّرِ ٱلۡمُؤۡمِنِينَ ﴾
[يُونس: 87]

Tidavumbulutsa Mau athu kwa Mose ndi m’bale wake ponena kuti: “Amangireni nyumba anthu anu m’dziko la Aiguputo ndipo mupange nyumba zanu kukhala malo opemphereramo. Pitirizani mapemphero ndipo muwauze nkhani yabwino anthu okhulupirira.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وأوحينا إلى موسى وأخيه أن تبوآ لقومكما بمصر بيوتا واجعلوا بيوتكم قبلة, باللغة نيانجا

﴿وأوحينا إلى موسى وأخيه أن تبوآ لقومكما بمصر بيوتا واجعلوا بيوتكم قبلة﴾ [يُونس: 87]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo tidavumbulutsa kwa Mûsa ndi m’bale wake mawu Athu (oti): “Apangireni nyumba anthu anu mu Eguputo ndipo nyumba zanu zichiteni kukhala misikiti (pakuti simungathe kukhala ndi misikiti yoonekera), ndipo pempherani Swala. Ndipo auze nkhani yabwino okhulupirira (kuti Allah awapatsa zabwino pa moyo wa dziko lapansi ndi pa tsiku lachimaliziro).”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek