×

Iye adati: “Oh inu anthu anga! Mukuona bwanji? Ngati ine ndili ndi 11:28 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Hud ⮕ (11:28) ayat 28 in Chichewa

11:28 Surah Hud ayat 28 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Hud ayat 28 - هُود - Page - Juz 12

﴿قَالَ يَٰقَوۡمِ أَرَءَيۡتُمۡ إِن كُنتُ عَلَىٰ بَيِّنَةٖ مِّن رَّبِّي وَءَاتَىٰنِي رَحۡمَةٗ مِّنۡ عِندِهِۦ فَعُمِّيَتۡ عَلَيۡكُمۡ أَنُلۡزِمُكُمُوهَا وَأَنتُمۡ لَهَا كَٰرِهُونَ ﴾
[هُود: 28]

Iye adati: “Oh inu anthu anga! Mukuona bwanji? Ngati ine ndili ndi umboni wochokera kwa Ambuye wanga ndiponso wandipatsa chifundo kuchokera kwa Iye, ndipo umboniwo wabisika kwa inu. Kodi ife tingakuumirizeni kuti mumvomere pamene mukunyansidwa nawo?”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قال ياقوم أرأيتم إن كنت على بينة من ربي وآتاني رحمة من, باللغة نيانجا

﴿قال ياقوم أرأيتم إن كنت على بينة من ربي وآتاني رحمة من﴾ [هُود: 28]

Khaled Ibrahim Betala
“(Iye) adati: “E inu anthu anga! Kodi muona bwanji ngati ndili ndi chisonyezo chowonekera chochokera kwa Mbuye wanga ndipo wandipatsa chifundo chochokera kwa Iye (monga uneneri), ndipo chabisika kwa inu, kodi tingakukakamizeni kuvomereza pomwe simukuchifuna?”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek