×

Ndipo kwa mtundu wa Aad, tidatumiza m’bale wawo Hud. Iye adati: “Oh 11:50 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Hud ⮕ (11:50) ayat 50 in Chichewa

11:50 Surah Hud ayat 50 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Hud ayat 50 - هُود - Page - Juz 12

﴿وَإِلَىٰ عَادٍ أَخَاهُمۡ هُودٗاۚ قَالَ يَٰقَوۡمِ ٱعۡبُدُواْ ٱللَّهَ مَا لَكُم مِّنۡ إِلَٰهٍ غَيۡرُهُۥٓۖ إِنۡ أَنتُمۡ إِلَّا مُفۡتَرُونَ ﴾
[هُود: 50]

Ndipo kwa mtundu wa Aad, tidatumiza m’bale wawo Hud. Iye adati: “Oh anthu anga! Pembedzani Mulungu. Inu mulibe mulungu wina kupatula Iye yekha. Ndithudi inu simuchita china chili chonse koma kupeka bodza basi.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وإلى عاد أخاهم هودا قال ياقوم اعبدوا الله ما لكم من إله, باللغة نيانجا

﴿وإلى عاد أخاهم هودا قال ياقوم اعبدوا الله ما لكم من إله﴾ [هُود: 50]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo anthu (amtundu) wa Âdi, tidawatumizira m’bale wawo Hûd. Adati: “E inu anthu anga! Pembedzani Allah! (Siyani kupembedza mafano). Mulibe mulungu wina koma Iye. Inu simuli kanthu koma ndinu opeka bodza (m’kunena kwanu kwakuti mafano ndi anzake a Allah).”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek