×

Iye adati: “Oh anthu anga! Ndiuzeni ngati ine ndili ndi umboni wokwanira 11:63 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Hud ⮕ (11:63) ayat 63 in Chichewa

11:63 Surah Hud ayat 63 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Hud ayat 63 - هُود - Page - Juz 12

﴿قَالَ يَٰقَوۡمِ أَرَءَيۡتُمۡ إِن كُنتُ عَلَىٰ بَيِّنَةٖ مِّن رَّبِّي وَءَاتَىٰنِي مِنۡهُ رَحۡمَةٗ فَمَن يَنصُرُنِي مِنَ ٱللَّهِ إِنۡ عَصَيۡتُهُۥۖ فَمَا تَزِيدُونَنِي غَيۡرَ تَخۡسِيرٖ ﴾
[هُود: 63]

Iye adati: “Oh anthu anga! Ndiuzeni ngati ine ndili ndi umboni wokwanira wochokera kwa Ambuye wanga ndipo Iye wandipatsa chisomo kuchokera kwa Iye, ndani angandipulumutse ine kuchokera ku chilango cha Mulungu ngati nditamunyoza? Inu simungaonjezere china chilichonse kwa ine koma kutayika.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قال ياقوم أرأيتم إن كنت على بينة من ربي وآتاني منه رحمة, باللغة نيانجا

﴿قال ياقوم أرأيتم إن كنت على بينة من ربي وآتاني منه رحمة﴾ [هُود: 63]

❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek