×

Ndipo kwa anthu a ku Midiyani tidawatumizira m’bale wawo Shoaib. Iye adati: 11:84 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Hud ⮕ (11:84) ayat 84 in Chichewa

11:84 Surah Hud ayat 84 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Hud ayat 84 - هُود - Page - Juz 12

﴿۞ وَإِلَىٰ مَدۡيَنَ أَخَاهُمۡ شُعَيۡبٗاۚ قَالَ يَٰقَوۡمِ ٱعۡبُدُواْ ٱللَّهَ مَا لَكُم مِّنۡ إِلَٰهٍ غَيۡرُهُۥۖ وَلَا تَنقُصُواْ ٱلۡمِكۡيَالَ وَٱلۡمِيزَانَۖ إِنِّيٓ أَرَىٰكُم بِخَيۡرٖ وَإِنِّيٓ أَخَافُ عَلَيۡكُمۡ عَذَابَ يَوۡمٖ مُّحِيطٖ ﴾
[هُود: 84]

Ndipo kwa anthu a ku Midiyani tidawatumizira m’bale wawo Shoaib. Iye adati: “oh Anthu anga! Pembedzani Mulungu, chifukwa inu mulibe mulungu wina koma Mulungu mmodzi yekha ndipo musapungule miyeso ya zinthu. Ine ndikuona kuti inu ndinu anthu a chuma. Ine, ndithudi, ndili kuchita mantha ndi chilango cha tsiku limene lidzakuzungulirani inu.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وإلى مدين أخاهم شعيبا قال ياقوم اعبدوا الله ما لكم من إله, باللغة نيانجا

﴿وإلى مدين أخاهم شعيبا قال ياقوم اعبدوا الله ما لكم من إله﴾ [هُود: 84]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo, ku Madiyan tidamtuma m’bale wawo Shuaib, iye adati: “E inu anthu anga! Pembedzani Allah; mulibe mulungu wina koma Iye. Ndipo musachepetse mulingo wa mbale ndi wasikelo (powapimira anthu), ine ndikukuonani kuti ndinu opeza bwino, ndipo ndikukuoperani chilango cha tsiku (lalikulu) lomwe lidzakuzingani.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek