×

“Oh anthu anga! Musalole kuti kusagwirizana kwanu ndi ine kuti kubweretse pa 11:89 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Hud ⮕ (11:89) ayat 89 in Chichewa

11:89 Surah Hud ayat 89 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Hud ayat 89 - هُود - Page - Juz 12

﴿وَيَٰقَوۡمِ لَا يَجۡرِمَنَّكُمۡ شِقَاقِيٓ أَن يُصِيبَكُم مِّثۡلُ مَآ أَصَابَ قَوۡمَ نُوحٍ أَوۡ قَوۡمَ هُودٍ أَوۡ قَوۡمَ صَٰلِحٖۚ وَمَا قَوۡمُ لُوطٖ مِّنكُم بِبَعِيدٖ ﴾
[هُود: 89]

“Oh anthu anga! Musalole kuti kusagwirizana kwanu ndi ine kuti kubweretse pa inu mavuto amene adadza pa anthu a Nowa, kapena pa anthu a Hud ndi Saleh ndiponso sikale pamene anthu a Loti adaonongeka.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وياقوم لا يجرمنكم شقاقي أن يصيبكم مثل ما أصاب قوم نوح أو, باللغة نيانجا

﴿وياقوم لا يجرمنكم شقاقي أن يصيبكم مثل ما أصاب قوم نوح أو﴾ [هُود: 89]

Khaled Ibrahim Betala
““Ndipo E inu anthu anga! Kutsutsana nane kusakuchimwitseni kuopera kuti chingakupezeni chonga chimene chidawapeza anthu a Nuh kapena anthu a Hûd kapenanso anthu a Swaleh; ndipo anthu a Luti sali kutali ndi inu.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek