×

Iye adati: “Ndiuzeni! Ngati ine ndili ndi umboni woonekera wochokera kwa Ambuye 11:88 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Hud ⮕ (11:88) ayat 88 in Chichewa

11:88 Surah Hud ayat 88 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Hud ayat 88 - هُود - Page - Juz 12

﴿قَالَ يَٰقَوۡمِ أَرَءَيۡتُمۡ إِن كُنتُ عَلَىٰ بَيِّنَةٖ مِّن رَّبِّي وَرَزَقَنِي مِنۡهُ رِزۡقًا حَسَنٗاۚ وَمَآ أُرِيدُ أَنۡ أُخَالِفَكُمۡ إِلَىٰ مَآ أَنۡهَىٰكُمۡ عَنۡهُۚ إِنۡ أُرِيدُ إِلَّا ٱلۡإِصۡلَٰحَ مَا ٱسۡتَطَعۡتُۚ وَمَا تَوۡفِيقِيٓ إِلَّا بِٱللَّهِۚ عَلَيۡهِ تَوَكَّلۡتُ وَإِلَيۡهِ أُنِيبُ ﴾
[هُود: 88]

Iye adati: “Ndiuzeni! Ngati ine ndili ndi umboni woonekera wochokera kwa Ambuye wanga ndipo Iye wandipatsa gawo labwino. Ine sindifuna kusemphana nanu pochita chinthu chimene ndili kukuletsani. Palibe chilichonse chimene ndifuna koma kukonza mmene ndingathere. Ndipo ulangizi wanga siubwera kuchokera kwa wina aliyense kupatula Mulungu. Mwa Iye ndaika chikhulupiriro changa ndipo kwa Iye ndiko ndimalapa.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قال ياقوم أرأيتم إن كنت على بينة من ربي ورزقني منه رزقا, باللغة نيانجا

﴿قال ياقوم أرأيتم إن كنت على بينة من ربي ورزقني منه رزقا﴾ [هُود: 88]

Khaled Ibrahim Betala
“(Iye) adati: “E inu anthu anga! Mukuona bwanji ngati ndili ndi umboni wowonekera wochokera kwa Mbuye wanga, ndipo nkundipatsa rizq labwino (lahalali) lochokera kwa Iye, (ndisiye zimenezi ndi kusankha njira yokhota)? Ndipo sindifuna kusiyana nanu pochita chimene ndakuletsani. Sindifuna china, koma kukonza mmene ndingathere; ndipo kupambana kwanga (pazimenezi) kuli kwa Allah. Kwa Iye ndatsamira, ndipo kwa Iye ndikutembenukira.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek