×

Ndipo pamene lamulo lathu lidadza tidamupulumutsa Shoaib, pamodzi ndi anzake onse amene 11:94 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Hud ⮕ (11:94) ayat 94 in Chichewa

11:94 Surah Hud ayat 94 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Hud ayat 94 - هُود - Page - Juz 12

﴿وَلَمَّا جَآءَ أَمۡرُنَا نَجَّيۡنَا شُعَيۡبٗا وَٱلَّذِينَ ءَامَنُواْ مَعَهُۥ بِرَحۡمَةٖ مِّنَّا وَأَخَذَتِ ٱلَّذِينَ ظَلَمُواْ ٱلصَّيۡحَةُ فَأَصۡبَحُواْ فِي دِيَٰرِهِمۡ جَٰثِمِينَ ﴾
[هُود: 94]

Ndipo pamene lamulo lathu lidadza tidamupulumutsa Shoaib, pamodzi ndi anzake onse amene anali wokhulupirira mwa chisomo chathu. Ndipo mkuwo waukulu udawaononga anthu onse ochita zoipa ndipo onse adali lambilambi m’nyumba zawo

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ولما جاء أمرنا نجينا شعيبا والذين آمنوا معه برحمة منا وأخذت الذين, باللغة نيانجا

﴿ولما جاء أمرنا نجينا شعيبا والذين آمنوا معه برحمة منا وأخذت الذين﴾ [هُود: 94]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo pamene lamulo Lathu lidadza, tidampulumutsa Shuaib pamodzi ndi amene adakhulupirira naye, mwachifundo Chathu. Ndipo amene adachita zoipa, phokoso lidawachotsa moyo, tero kudawachera m’nyumba zawo ali lambilambi (atafa)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek