×

“oh anthu anga! Chitani chimene mufuna kuti muchite, nanenso ndidzachita zanga. Inu 11:93 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Hud ⮕ (11:93) ayat 93 in Chichewa

11:93 Surah Hud ayat 93 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Hud ayat 93 - هُود - Page - Juz 12

﴿وَيَٰقَوۡمِ ٱعۡمَلُواْ عَلَىٰ مَكَانَتِكُمۡ إِنِّي عَٰمِلٞۖ سَوۡفَ تَعۡلَمُونَ مَن يَأۡتِيهِ عَذَابٞ يُخۡزِيهِ وَمَنۡ هُوَ كَٰذِبٞۖ وَٱرۡتَقِبُوٓاْ إِنِّي مَعَكُمۡ رَقِيبٞ ﴾
[هُود: 93]

“oh anthu anga! Chitani chimene mufuna kuti muchite, nanenso ndidzachita zanga. Inu mudzadziwa kuti ndani adzalangidwa ndi chilango chochititsa manyazi ndiponso kuti kodi ndani amene ali kunama! Ndithudi dikirani nanenso ndili kudikira pamodzi ndi inu.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وياقوم اعملوا على مكانتكم إني عامل سوف تعلمون من يأتيه عذاب يخزيه, باللغة نيانجا

﴿وياقوم اعملوا على مكانتكم إني عامل سوف تعلمون من يأتيه عذاب يخزيه﴾ [هُود: 93]

Khaled Ibrahim Betala
““Ndipo E anthu anga! Chitani (zimene mufuna) mmene mungathere; inenso ndichita chimodzimodzi (mmene ndingathere). Posachedwapa mudziwa ndani chimufike chilango chomsambula, ndipo ndani wabodza. Ndipo dikirani inenso ndidikira pamodzi ndi inu.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek