×

Ndithudi mkazi adamufunitsitsa Yosefe ndipo nayenso akadamufuna iye pakadapanda kuti adaona umboni 12:24 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yusuf ⮕ (12:24) ayat 24 in Chichewa

12:24 Surah Yusuf ayat 24 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yusuf ayat 24 - يُوسُف - Page - Juz 12

﴿وَلَقَدۡ هَمَّتۡ بِهِۦۖ وَهَمَّ بِهَا لَوۡلَآ أَن رَّءَا بُرۡهَٰنَ رَبِّهِۦۚ كَذَٰلِكَ لِنَصۡرِفَ عَنۡهُ ٱلسُّوٓءَ وَٱلۡفَحۡشَآءَۚ إِنَّهُۥ مِنۡ عِبَادِنَا ٱلۡمُخۡلَصِينَ ﴾
[يُوسُف: 24]

Ndithudi mkazi adamufunitsitsa Yosefe ndipo nayenso akadamufuna iye pakadapanda kuti adaona umboni wochokera kwa Ambuye ake. Ife tidatero ndi cholinga chomuteteza ku chinthu chochititsa manyazi ndiponso choipa. Ndithudi iye adali mmodzi wa akapolo athu otsogozedwa

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ولقد همت به وهم بها لولا أن رأى برهان ربه كذلك لنصرف, باللغة نيانجا

﴿ولقد همت به وهم بها لولا أن رأى برهان ربه كذلك لنصرف﴾ [يُوسُف: 24]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo (mkaziyo) adaikira mtima pa iye (kuti achite naye kanthu), ndipo naye (Yûsuf) adaikira mtima pa iye (kuti ammenye). Pakadapanda kuona chisonyezo cha Mbuye wake (chakumzindikiritsa kuti asatero, akadammenya. Koma adamthawa). Tidachita izi kuti timchotsere chinthu choipa ndi chauve; ndithudi, iye adali mwa akapolo athu oyeretsedwa
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek