×

Ndipo pamene mwamuna wake adaona kuti malaya ake adang’ambika kumbuyo, iye adati, 12:28 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yusuf ⮕ (12:28) ayat 28 in Chichewa

12:28 Surah Yusuf ayat 28 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yusuf ayat 28 - يُوسُف - Page - Juz 12

﴿فَلَمَّا رَءَا قَمِيصَهُۥ قُدَّ مِن دُبُرٖ قَالَ إِنَّهُۥ مِن كَيۡدِكُنَّۖ إِنَّ كَيۡدَكُنَّ عَظِيمٞ ﴾
[يُوسُف: 28]

Ndipo pamene mwamuna wake adaona kuti malaya ake adang’ambika kumbuyo, iye adati, “Ichi ndi chimodzi cha ukamberembere wanu wa amayi. Ndithudi ukamberembere wanu ndi waukulu.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فلما رأى قميصه قد من دبر قال إنه من كيدكن إن كيدكن, باللغة نيانجا

﴿فلما رأى قميصه قد من دبر قال إنه من كيدكن إن كيدكن﴾ [يُوسُف: 28]

Khaled Ibrahim Betala
“Choncho (mwamuna uja) pamene adaona mkanjo wake (wa Yûsuf) utang’ambidwa chakumbuyo, (adadziwa kuti Yûsuf ndi amene amafuna kugwiliridwa), adati: “Ndithudi, izi ndi ndale zanu akazi. Ndithu ndale zanu ndi zazikulu (iwe mkazi wanga ndi amene udatsimikiza kuchita choipa ndi mnyamatayu).”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek