×

“Oh Yosefe munthu wa choonadi! Tiuzeni za ng’ombe zisanu ndi ziwiri zonenepa 12:46 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yusuf ⮕ (12:46) ayat 46 in Chichewa

12:46 Surah Yusuf ayat 46 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yusuf ayat 46 - يُوسُف - Page - Juz 12

﴿يُوسُفُ أَيُّهَا ٱلصِّدِّيقُ أَفۡتِنَا فِي سَبۡعِ بَقَرَٰتٖ سِمَانٖ يَأۡكُلُهُنَّ سَبۡعٌ عِجَافٞ وَسَبۡعِ سُنۢبُلَٰتٍ خُضۡرٖ وَأُخَرَ يَابِسَٰتٖ لَّعَلِّيٓ أَرۡجِعُ إِلَى ٱلنَّاسِ لَعَلَّهُمۡ يَعۡلَمُونَ ﴾
[يُوسُف: 46]

“Oh Yosefe munthu wa choonadi! Tiuzeni za ng’ombe zisanu ndi ziwiri zonenepa zimene zinali kudyedwa ndi ng’ombe zisanu ndi ziwiri zoonda ndiponso za ngala zisanu ndi ziwiri zaziwisi ndi ngala zisanu ndi ziwiri zouma, kuti ndibwerere ndikawauze anthu kuti akadziwe tanthauzo lake?”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: يوسف أيها الصديق أفتنا في سبع بقرات سمان يأكلهن سبع عجاف وسبع, باللغة نيانجا

﴿يوسف أيها الصديق أفتنا في سبع بقرات سمان يأكلهن سبع عجاف وسبع﴾ [يُوسُف: 46]

Khaled Ibrahim Betala
“(Adanka kundende ndikumpempha Yûsuf chikhululuko chifukwa cha kuiwala kwake. Ndipo adati): “Yûsuf! E iwe woona! Tiuze za ng’ombe zisanu ndi ziwiri zonenepa zikudyedwa ndi zisanu ndi ziwiri zoonda, ndi ngala zisanu ndi ziwiri zaziwisi ndi zina zouma; kuti ine ndibwelere kwa anthu kuti akadziwe.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek