×

Ndipo pamene iwo adatsekula katundu wawo, adapeza kuti ndalama zawo zabwezedwa kwa 12:65 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yusuf ⮕ (12:65) ayat 65 in Chichewa

12:65 Surah Yusuf ayat 65 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yusuf ayat 65 - يُوسُف - Page - Juz 13

﴿وَلَمَّا فَتَحُواْ مَتَٰعَهُمۡ وَجَدُواْ بِضَٰعَتَهُمۡ رُدَّتۡ إِلَيۡهِمۡۖ قَالُواْ يَٰٓأَبَانَا مَا نَبۡغِيۖ هَٰذِهِۦ بِضَٰعَتُنَا رُدَّتۡ إِلَيۡنَاۖ وَنَمِيرُ أَهۡلَنَا وَنَحۡفَظُ أَخَانَا وَنَزۡدَادُ كَيۡلَ بَعِيرٖۖ ذَٰلِكَ كَيۡلٞ يَسِيرٞ ﴾
[يُوسُف: 65]

Ndipo pamene iwo adatsekula katundu wawo, adapeza kuti ndalama zawo zabwezedwa kwa iwo. Iwo adati, “oh Atate athu! Kodi ndi chiyani chimene tingafunenso? Nazi ndalama zathu zabwezedwa kwa ife motero tidzapeza chakudya chambiri cha mabanja athu. Ndiponso tidzamusamala m’bale wathu ndi kuonjezera muyeso wokwana kunyamulidwa ndi ngamira imodzi. Umenewu ndiwo muyeso wochepa.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ولما فتحوا متاعهم وجدوا بضاعتهم ردت إليهم قالوا ياأبانا ما نبغي هذه, باللغة نيانجا

﴿ولما فتحوا متاعهم وجدوا بضاعتهم ردت إليهم قالوا ياأبانا ما نبغي هذه﴾ [يُوسُف: 65]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo pamene adatsekula katundu wawo, adapeza chuma chawo chabwezedwa kwa iwo. Adati: “E bambo wathu! Tingafunenso chiyani (kwa munthu waufuluyu)? Ichi chuma chathu chabwezedwa kwa ife; ndipo tikabweretsa chakudya chothandizira mawanja athu; ndipo m’bale wathu tikamsunga; tikapezanso muyeso wangamira imodzi yoonjezera. Umenewu ndi mlingo wochepa (kwa mfumu ya ufuluyo).”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek