×

Atumwi awo adati kwa iwo, “Ife tili anthu ngati inu nomwe koma 14:11 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ibrahim ⮕ (14:11) ayat 11 in Chichewa

14:11 Surah Ibrahim ayat 11 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ibrahim ayat 11 - إبراهِيم - Page - Juz 13

﴿قَالَتۡ لَهُمۡ رُسُلُهُمۡ إِن نَّحۡنُ إِلَّا بَشَرٞ مِّثۡلُكُمۡ وَلَٰكِنَّ ٱللَّهَ يَمُنُّ عَلَىٰ مَن يَشَآءُ مِنۡ عِبَادِهِۦۖ وَمَا كَانَ لَنَآ أَن نَّأۡتِيَكُم بِسُلۡطَٰنٍ إِلَّا بِإِذۡنِ ٱللَّهِۚ وَعَلَى ٱللَّهِ فَلۡيَتَوَكَّلِ ٱلۡمُؤۡمِنُونَ ﴾
[إبراهِيم: 11]

Atumwi awo adati kwa iwo, “Ife tili anthu ngati inu nomwe koma Mulungu amakhazikitsa chisomo chake pa ena mwa akapolo ake amene Iye wawasankha. Ife sitingathe kukupatsani chizindikiro pokhapokha ngati Mulungu afuna. Mwa Mulungu yekha onse okhulupirira aike chikhulupiriro chawo.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قالت لهم رسلهم إن نحن إلا بشر مثلكم ولكن الله يمن على, باللغة نيانجا

﴿قالت لهم رسلهم إن نحن إلا بشر مثلكم ولكن الله يمن على﴾ [إبراهِيم: 11]

Khaled Ibrahim Betala
“Atumiki awo adati kwa iwo: “(Zoonadi), ife ndife anthu ngati inu, koma Allah amamchitira zabwino yemwe wamfuna mwa akapolo ake. Ndipo ife tilibe nyonga zokubweretserani chisonyezo koma mwachilolezo cha Allah. Ndipo kwa Allah yekha atsamire okhulupirira onse.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek