×

Atumwi awo adati, “Chiyani! Kodi pangakhale chikayiko pa Mulungu, Namalenga wa kumwamba 14:10 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ibrahim ⮕ (14:10) ayat 10 in Chichewa

14:10 Surah Ibrahim ayat 10 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ibrahim ayat 10 - إبراهِيم - Page - Juz 13

﴿۞ قَالَتۡ رُسُلُهُمۡ أَفِي ٱللَّهِ شَكّٞ فَاطِرِ ٱلسَّمَٰوَٰتِ وَٱلۡأَرۡضِۖ يَدۡعُوكُمۡ لِيَغۡفِرَ لَكُم مِّن ذُنُوبِكُمۡ وَيُؤَخِّرَكُمۡ إِلَىٰٓ أَجَلٖ مُّسَمّٗىۚ قَالُوٓاْ إِنۡ أَنتُمۡ إِلَّا بَشَرٞ مِّثۡلُنَا تُرِيدُونَ أَن تَصُدُّونَا عَمَّا كَانَ يَعۡبُدُ ءَابَآؤُنَا فَأۡتُونَا بِسُلۡطَٰنٖ مُّبِينٖ ﴾
[إبراهِيم: 10]

Atumwi awo adati, “Chiyani! Kodi pangakhale chikayiko pa Mulungu, Namalenga wa kumwamba ndi dziko lapansi? Iye akukuitanani kuti akukhululukireni machimo anu ndi kukusungani mpaka pa nthawi yomwe idaikidwa.” Iwo adati, “Inu simuli ena, koma anthu ngati ife. Inu mufuna kutiletsa zimene makolo athu anali kupembedza. Tipatseni umboni weniweni wooneka.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قالت رسلهم أفي الله شك فاطر السموات والأرض يدعوكم ليغفر لكم من, باللغة نيانجا

﴿قالت رسلهم أفي الله شك فاطر السموات والأرض يدعوكم ليغفر لكم من﴾ [إبراهِيم: 10]

Khaled Ibrahim Betala
“Atumiki awo adati: “Kodi mwa Allah, Mlengi wa thambo ndi nthaka muli chikaiko? Iye akukuitanani kuti akukhululukireni machimo anu, ndi kuti (mukakhulupirira) akupatseni nthawi (pokutalikitsirani moyo wanu) kufikira pa nthawi yoyikidwa.” Adati: “Inu sikanthu kena koma ndinu anthu ngati ife. Mungofuna kutitsekereza ku zimene ankazipembedza makolo athu; choncho tibweretsereni umboni woonekera.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek