×

Usaganize kuti Mulungu sadziwa ntchito za anthu ochita zoipa koma Iye akungowasiya 14:42 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ibrahim ⮕ (14:42) ayat 42 in Chichewa

14:42 Surah Ibrahim ayat 42 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ibrahim ayat 42 - إبراهِيم - Page - Juz 13

﴿وَلَا تَحۡسَبَنَّ ٱللَّهَ غَٰفِلًا عَمَّا يَعۡمَلُ ٱلظَّٰلِمُونَۚ إِنَّمَا يُؤَخِّرُهُمۡ لِيَوۡمٖ تَشۡخَصُ فِيهِ ٱلۡأَبۡصَٰرُ ﴾
[إبراهِيم: 42]

Usaganize kuti Mulungu sadziwa ntchito za anthu ochita zoipa koma Iye akungowasiya mpaka patsiku limene maso awo adzaona motuzuka

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ولا تحسبن الله غافلا عما يعمل الظالمون إنما يؤخرهم ليوم تشخص فيه, باللغة نيانجا

﴿ولا تحسبن الله غافلا عما يعمل الظالمون إنما يؤخرهم ليوم تشخص فيه﴾ [إبراهِيم: 42]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo usaganize kuti Allah waiwala zomwe akuchita oipa. Ndithudi, Iye akuwalekelera chabe mpaka tsiku lomwe maso awo adzatong’oke (chifukwa cha mantha)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek