×

Ndipo ngati Ife tikadatsekula khomo lakumwamba, iwo ndi kumakwera kumwamba mosalekeza 15:14 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-hijr ⮕ (15:14) ayat 14 in Chichewa

15:14 Surah Al-hijr ayat 14 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-hijr ayat 14 - الحِجر - Page - Juz 14

﴿وَلَوۡ فَتَحۡنَا عَلَيۡهِم بَابٗا مِّنَ ٱلسَّمَآءِ فَظَلُّواْ فِيهِ يَعۡرُجُونَ ﴾
[الحِجر: 14]

Ndipo ngati Ife tikadatsekula khomo lakumwamba, iwo ndi kumakwera kumwamba mosalekeza

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ولو فتحنا عليهم بابا من السماء فظلوا فيه يعرجون, باللغة نيانجا

﴿ولو فتحنا عليهم بابا من السماء فظلوا فيه يعرجون﴾ [الحِجر: 14]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo tikadawatsekulira (awa osakhulupirira) khomo lakumwamba ndipo nkukhala akukwera m’menemo (ndi kutsika monga momwe amafunira kuti zimenezo zikhale chozizwitsa cha Mtumiki)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek