×

Satana adati, “Oh Ambuye wanga! Popeza Inuyo mwandisocheretsa ine, ndithudi, ndidzawasalalitsira njira 15:39 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-hijr ⮕ (15:39) ayat 39 in Chichewa

15:39 Surah Al-hijr ayat 39 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-hijr ayat 39 - الحِجر - Page - Juz 14

﴿قَالَ رَبِّ بِمَآ أَغۡوَيۡتَنِي لَأُزَيِّنَنَّ لَهُمۡ فِي ٱلۡأَرۡضِ وَلَأُغۡوِيَنَّهُمۡ أَجۡمَعِينَ ﴾
[الحِجر: 39]

Satana adati, “Oh Ambuye wanga! Popeza Inuyo mwandisocheretsa ine, ndithudi, ndidzawasalalitsira njira yautchimo anthu onse padziko lapansi, ndithudi onse ndidzawasocheretsa

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قال رب بما أغويتني لأزينن لهم في الأرض ولأغوينهم أجمعين, باللغة نيانجا

﴿قال رب بما أغويتني لأزينن لهم في الأرض ولأغوينهم أجمعين﴾ [الحِجر: 39]

Khaled Ibrahim Betala
“(Satana) adati: “Mbuye wanga! Pakuti mwanena kuti ndine wosokera, choncho ndikawakometsera za m’dziko (kufikira kuti akakulakwireni), ndithu ndikawasokeretsa onse.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek