×

Nena, “Mulungu amadziwa kwambiri mmene adakhalira. Kudziwa zinsinsi zonse za kumwamba ndi 18:26 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Kahf ⮕ (18:26) ayat 26 in Chichewa

18:26 Surah Al-Kahf ayat 26 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Kahf ayat 26 - الكَهف - Page - Juz 15

﴿قُلِ ٱللَّهُ أَعۡلَمُ بِمَا لَبِثُواْۖ لَهُۥ غَيۡبُ ٱلسَّمَٰوَٰتِ وَٱلۡأَرۡضِۖ أَبۡصِرۡ بِهِۦ وَأَسۡمِعۡۚ مَا لَهُم مِّن دُونِهِۦ مِن وَلِيّٖ وَلَا يُشۡرِكُ فِي حُكۡمِهِۦٓ أَحَدٗا ﴾
[الكَهف: 26]

Nena, “Mulungu amadziwa kwambiri mmene adakhalira. Kudziwa zinsinsi zonse za kumwamba ndi za dziko lapansi ndi kwake. Oh! Iye amapenyetsetsa ndipo amamvetsetsa. Iwo alibe wina woti awasamale oposa Mulungu. Ndipo Iye samuphatikiza wina aliyense mu ulamuliro wake.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قل الله أعلم بما لبثوا له غيب السموات والأرض أبصر به وأسمع, باللغة نيانجا

﴿قل الله أعلم بما لبثوا له غيب السموات والأرض أبصر به وأسمع﴾ [الكَهف: 26]

Khaled Ibrahim Betala
“Nena: “Allah akudziwa bwinobwino nyengo imene (iwo) adakhala; zobisika za kumwamba ndi za pansi nza Iye (Allah basi); taona Allah kuonetsetsa! Taona Allah kumvetsetsa! (Allah Ngoona chilichonse, ndipo Ngwakumva chilichonse). Ndipo iwo alibe mtetezi popanda Iye (Allah); ndipo Iye sagawira aliyense udindo Wake wakulamula
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek