×

“Ndipo ine sindikhulupirira kuti ola la chionongeko lidzadza. Ndipo ngakhale nditabwezedwa kwa 18:36 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Kahf ⮕ (18:36) ayat 36 in Chichewa

18:36 Surah Al-Kahf ayat 36 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Kahf ayat 36 - الكَهف - Page - Juz 15

﴿وَمَآ أَظُنُّ ٱلسَّاعَةَ قَآئِمَةٗ وَلَئِن رُّدِدتُّ إِلَىٰ رَبِّي لَأَجِدَنَّ خَيۡرٗا مِّنۡهَا مُنقَلَبٗا ﴾
[الكَهف: 36]

“Ndipo ine sindikhulupirira kuti ola la chionongeko lidzadza. Ndipo ngakhale nditabwezedwa kwa Ambuye wanga, ine ndikapeza malo abwino oposa awa.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وما أظن الساعة قائمة ولئن رددت إلى ربي لأجدن خيرا منها منقلبا, باللغة نيانجا

﴿وما أظن الساعة قائمة ولئن رددت إلى ربي لأجدن خيرا منها منقلبا﴾ [الكَهف: 36]

Khaled Ibrahim Betala
““Ndiponso sindiganiza kuti Qiyâma (chimaliziro) idzachitikadi. Ngati (itapezekadi Kiyamayo), ine nkubwezedwa kwa Mbuye wanga, ndithu ndikapeza malo abwino wobwererako kuposa awa. (Monga momwe ndapezera mwayi kuno, ukonso ndikapeza, ngati Kiyamayo ilikodi).”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek