×

Kodiwolakwakwambirindanikuposa munthu amene akakumbutsidwa mavesi a Ambuye wake iye amawakana ndi kuiwala 18:57 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Kahf ⮕ (18:57) ayat 57 in Chichewa

18:57 Surah Al-Kahf ayat 57 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Kahf ayat 57 - الكَهف - Page - Juz 15

﴿وَمَنۡ أَظۡلَمُ مِمَّن ذُكِّرَ بِـَٔايَٰتِ رَبِّهِۦ فَأَعۡرَضَ عَنۡهَا وَنَسِيَ مَا قَدَّمَتۡ يَدَاهُۚ إِنَّا جَعَلۡنَا عَلَىٰ قُلُوبِهِمۡ أَكِنَّةً أَن يَفۡقَهُوهُ وَفِيٓ ءَاذَانِهِمۡ وَقۡرٗاۖ وَإِن تَدۡعُهُمۡ إِلَى ٱلۡهُدَىٰ فَلَن يَهۡتَدُوٓاْ إِذًا أَبَدٗا ﴾
[الكَهف: 57]

Kodiwolakwakwambirindanikuposa munthu amene akakumbutsidwa mavesi a Ambuye wake iye amawakana ndi kuiwala zimene manja ake atsogoza? Ife taika zophimba mitima yawo kuti asazindikire ndipo tatseka m’makutu mwawo. Ndipo ngati iwe utawaitana iwo kuti atsatire njira yoyenera, iwo sadzatsogozedwa

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ومن أظلم ممن ذكر بآيات ربه فأعرض عنها ونسي ما قدمت يداه, باللغة نيانجا

﴿ومن أظلم ممن ذكر بآيات ربه فأعرض عنها ونسي ما قدمت يداه﴾ [الكَهف: 57]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndindani woipitsitsa kwabasi woposa yemwe akukumbutsidwa ndi Ayah za Mbuye wake, koma iye nkuzinyoza, ndipo nkuiwala (zoipa) zimene manja ake adatsogoza? Ndithu Ife taika m’mitima mwawo zitsekelero kuti asazizindikire. Ndiponso m’makutu mwawo mwalemedwa ndi ugonthi. Ndipo ukawaitanira kuchiongoko (choonadi), salola kuongoka ngakhale pang’ono
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek