×

Ndipo Ambuye wako ndi wokhululukira kwambiri ndi Mwini chisoni. Iye akadafuna kuwalanga 18:58 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Kahf ⮕ (18:58) ayat 58 in Chichewa

18:58 Surah Al-Kahf ayat 58 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Kahf ayat 58 - الكَهف - Page - Juz 15

﴿وَرَبُّكَ ٱلۡغَفُورُ ذُو ٱلرَّحۡمَةِۖ لَوۡ يُؤَاخِذُهُم بِمَا كَسَبُواْ لَعَجَّلَ لَهُمُ ٱلۡعَذَابَۚ بَل لَّهُم مَّوۡعِدٞ لَّن يَجِدُواْ مِن دُونِهِۦ مَوۡئِلٗا ﴾
[الكَهف: 58]

Ndipo Ambuye wako ndi wokhululukira kwambiri ndi Mwini chisoni. Iye akadafuna kuwalanga chifukwa cha machimo amene achita, ndithudi, Iye akadawafulumizitsira chilango chawo. Koma iwo ali ndi nthawi yawo ndipo sadzapeza kothawirako

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وربك الغفور ذو الرحمة لو يؤاخذهم بما كسبوا لعجل لهم العذاب بل, باللغة نيانجا

﴿وربك الغفور ذو الرحمة لو يؤاخذهم بما كسبوا لعجل لهم العذاب بل﴾ [الكَهف: 58]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo Mbuye wako Ngokhululuka kwambiri mwini chifundo. Ndipo akadawathira m’dzanja pa zoipa zomwe akhala akuchita, ndiye kuti ndithu akadawapatsa chilango mwachangu; koma iwo ali nalo lonjezo ndipo sadzapeza pothawira paliponse ndikulipewa
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek