×

Iye adati, “Mphamvu zomangira linga zimene Ambuye wanga wandipatsa ndi zabwino. Choncho 18:95 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Kahf ⮕ (18:95) ayat 95 in Chichewa

18:95 Surah Al-Kahf ayat 95 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Kahf ayat 95 - الكَهف - Page - Juz 16

﴿قَالَ مَا مَكَّنِّي فِيهِ رَبِّي خَيۡرٞ فَأَعِينُونِي بِقُوَّةٍ أَجۡعَلۡ بَيۡنَكُمۡ وَبَيۡنَهُمۡ رَدۡمًا ﴾
[الكَهف: 95]

Iye adati, “Mphamvu zomangira linga zimene Ambuye wanga wandipatsa ndi zabwino. Choncho ndithandizeni ndi anthu amphamvu ogwira ntchito kuti ndimange linga pakati pa inu ndi iwo.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قال ما مكني فيه ربي خير فأعينوني بقوة أجعل بينكم وبينهم ردما, باللغة نيانجا

﴿قال ما مكني فيه ربي خير فأعينوني بقوة أجعل بينكم وبينهم ردما﴾ [الكَهف: 95]

Khaled Ibrahim Betala
“(Iye) adati: “Zomwe Mbuye wanga wandipatsa ndi zabwino. Choncho ndithandizeni ndi mphamvu zanu (zonse pantchito imeneyi) ndiika chotchinga cholimba pakati panu ndi pakati pawo.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek