Quran with Chichewa translation - Surah Maryam ayat 29 - مَريَم - Page - Juz 16
﴿فَأَشَارَتۡ إِلَيۡهِۖ قَالُواْ كَيۡفَ نُكَلِّمُ مَن كَانَ فِي ٱلۡمَهۡدِ صَبِيّٗا ﴾
[مَريَم: 29]
﴿فأشارت إليه قالوا كيف نكلم من كان في المهد صبيا﴾ [مَريَم: 29]
Khaled Ibrahim Betala “(Mariya sadawayankhe) koma adaloza kwa iye (mwanayo kuti ayankhule naye). Ndipo iwo adati: “Timuyankhula chotani mwana yemwe ali m’chikuta?” |