×

Ndipo pamene inu mukwaniritsa mapemphero anu a Hajji, kumbukirani Mulungu monga momwe 2:200 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Baqarah ⮕ (2:200) ayat 200 in Chichewa

2:200 Surah Al-Baqarah ayat 200 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Baqarah ayat 200 - البَقَرَة - Page - Juz 2

﴿فَإِذَا قَضَيۡتُم مَّنَٰسِكَكُمۡ فَٱذۡكُرُواْ ٱللَّهَ كَذِكۡرِكُمۡ ءَابَآءَكُمۡ أَوۡ أَشَدَّ ذِكۡرٗاۗ فَمِنَ ٱلنَّاسِ مَن يَقُولُ رَبَّنَآ ءَاتِنَا فِي ٱلدُّنۡيَا وَمَا لَهُۥ فِي ٱلۡأٓخِرَةِ مِنۡ خَلَٰقٖ ﴾
[البَقَرَة: 200]

Ndipo pamene inu mukwaniritsa mapemphero anu a Hajji, kumbukirani Mulungu monga momwe mumakumbukira makolo anu kapena kuposa pamenepo. Ndipo pakati pawo pali iye amene amanena kuti: “Ambuye wathu! Tipatseni zabwino m’dziko lapansi!” Ndipo munthu wotere sadzakhala ndi gawo m’moyo umene uli nkudza

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فإذا قضيتم مناسككم فاذكروا الله كذكركم آباءكم أو أشد ذكرا فمن الناس, باللغة نيانجا

﴿فإذا قضيتم مناسككم فاذكروا الله كذكركم آباءكم أو أشد ذكرا فمن الناس﴾ [البَقَرَة: 200]

❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek