×

Iwo adzakhala m’menemo mpaka kalekale ndipo zidzakhala zoipa kwambiri kwa iwo osenza 20:101 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ta-Ha ⮕ (20:101) ayat 101 in Chichewa

20:101 Surah Ta-Ha ayat 101 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ta-Ha ayat 101 - طه - Page - Juz 16

﴿خَٰلِدِينَ فِيهِۖ وَسَآءَ لَهُمۡ يَوۡمَ ٱلۡقِيَٰمَةِ حِمۡلٗا ﴾
[طه: 101]

Iwo adzakhala m’menemo mpaka kalekale ndipo zidzakhala zoipa kwambiri kwa iwo osenza katundu wotereyu tsiku la kuuka kwa kufa

❮ Previous Next ❯

ترجمة: خالدين فيه وساء لهم يوم القيامة حملا, باللغة نيانجا

﴿خالدين فيه وساء لهم يوم القيامة حملا﴾ [طه: 101]

Khaled Ibrahim Betala
“Adzakhala m’menemo m’chilango. Ndipo ndi zoipa zedi (kwa anthu) kusenza mitolo (imeneyo) tsiku la Qiyâma
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek