×

Ndipo pakati pa anthu pamakhala munthu amene amampembedza Mulungu mokayikira. Zikapezeka zabwino 22:11 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-hajj ⮕ (22:11) ayat 11 in Chichewa

22:11 Surah Al-hajj ayat 11 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-hajj ayat 11 - الحج - Page - Juz 17

﴿وَمِنَ ٱلنَّاسِ مَن يَعۡبُدُ ٱللَّهَ عَلَىٰ حَرۡفٖۖ فَإِنۡ أَصَابَهُۥ خَيۡرٌ ٱطۡمَأَنَّ بِهِۦۖ وَإِنۡ أَصَابَتۡهُ فِتۡنَةٌ ٱنقَلَبَ عَلَىٰ وَجۡهِهِۦ خَسِرَ ٱلدُّنۡيَا وَٱلۡأٓخِرَةَۚ ذَٰلِكَ هُوَ ٱلۡخُسۡرَانُ ٱلۡمُبِينُ ﴾
[الحج: 11]

Ndipo pakati pa anthu pamakhala munthu amene amampembedza Mulungu mokayikira. Zikapezeka zabwino amakhala wokhutitsidwa ndi izo koma ngati mavuto amugwera amatembenuka motero; iye amataya zabwino za m’moyo uno ndi za m’moyo umene uli nkudza. Kumeneko ndiko kulephera koonekeratu

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ومن الناس من يعبد الله على حرف فإن أصابه خير اطمأن به, باللغة نيانجا

﴿ومن الناس من يعبد الله على حرف فإن أصابه خير اطمأن به﴾ [الحج: 11]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo alipo wina mwa anthu amene akupembedza Allah cham’mphepete (mwachipembedzo). Chabwino chikampeza amatonthola nacho; koma masautso akamufika, amatembenuka ndi nkhope yake (posiya chikhulupiliro mwa Allah. Choncho) waluza moyo wa dziko lapansi ndi moyo wa tsiku la chimaliziro; kumeneko ndiko kuluza koonekera
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek