×

Tsiku limene mudzachiona, mkazi aliyense woyamwitsa adzaiwala mwana wake ndipo mkazi aliyense 22:2 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-hajj ⮕ (22:2) ayat 2 in Chichewa

22:2 Surah Al-hajj ayat 2 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-hajj ayat 2 - الحج - Page - Juz 17

﴿يَوۡمَ تَرَوۡنَهَا تَذۡهَلُ كُلُّ مُرۡضِعَةٍ عَمَّآ أَرۡضَعَتۡ وَتَضَعُ كُلُّ ذَاتِ حَمۡلٍ حَمۡلَهَا وَتَرَى ٱلنَّاسَ سُكَٰرَىٰ وَمَا هُم بِسُكَٰرَىٰ وَلَٰكِنَّ عَذَابَ ٱللَّهِ شَدِيدٞ ﴾
[الحج: 2]

Tsiku limene mudzachiona, mkazi aliyense woyamwitsa adzaiwala mwana wake ndipo mkazi aliyense wapakati adzabala nthawi yake isanafike ndipo udzawaona anthu ngati oledzera pamene sali oledzera; koma chilango cha Mulungu chidzakhala chowawa

❮ Previous Next ❯

ترجمة: يوم ترونها تذهل كل مرضعة عما أرضعت وتضع كل ذات حمل حملها, باللغة نيانجا

﴿يوم ترونها تذهل كل مرضعة عما أرضعت وتضع كل ذات حمل حملها﴾ [الحج: 2]

Khaled Ibrahim Betala
“Tsiku limene mudzaione (Qiyâmayo), mkazi aliyense woyamwitsa adzaiwala (mwana wake) womuyamwitsa, ndipo (mkazi) aliyense wapakati adzataya pakati pake; ndipo udzawaona anthu ataledzera, pomwe sadaledzere; koma ndi chilango chaukali cha Allah (chimene chawapeza)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek