×

Si mnofu wawo kapena magazi awo amene amafika kwa Mulungu koma ndi 22:37 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-hajj ⮕ (22:37) ayat 37 in Chichewa

22:37 Surah Al-hajj ayat 37 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-hajj ayat 37 - الحج - Page - Juz 17

﴿لَن يَنَالَ ٱللَّهَ لُحُومُهَا وَلَا دِمَآؤُهَا وَلَٰكِن يَنَالُهُ ٱلتَّقۡوَىٰ مِنكُمۡۚ كَذَٰلِكَ سَخَّرَهَا لَكُمۡ لِتُكَبِّرُواْ ٱللَّهَ عَلَىٰ مَا هَدَىٰكُمۡۗ وَبَشِّرِ ٱلۡمُحۡسِنِينَ ﴾
[الحج: 37]

Si mnofu wawo kapena magazi awo amene amafika kwa Mulungu koma ndi kumvera Mulungu kumene kumafika kwa Iye. Kotero Ife tazilamula kuti zizikutumikirani kuti muzilemekeza Mulungu chifukwa chokulangizani inu njira yoyenera. Auze nkhani yabwino anthu angwiro

❮ Previous Next ❯

ترجمة: لن ينال الله لحومها ولا دماؤها ولكن يناله التقوى منكم كذلك سخرها, باللغة نيانجا

﴿لن ينال الله لحومها ولا دماؤها ولكن يناله التقوى منكم كذلك سخرها﴾ [الحج: 37]

Khaled Ibrahim Betala
“(Nyamazo) Allah siimfika minofu yake ngakhale magazi ake, koma kuopa kuchokera mwa inu ndiko kumene kumamfika; momwemo wazichita (nyamazo) kukhala zogonjera inu kuti mumlemekeze Allah chifukwa cha kukuongolaniku. Auze nkhani yabwino ochita zabwino
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek