×

Ndi nyama zina tidazipanga kukhala ngati zina mwa zizindikiro za Mulungu ndipo 22:36 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-hajj ⮕ (22:36) ayat 36 in Chichewa

22:36 Surah Al-hajj ayat 36 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-hajj ayat 36 - الحج - Page - Juz 17

﴿وَٱلۡبُدۡنَ جَعَلۡنَٰهَا لَكُم مِّن شَعَٰٓئِرِ ٱللَّهِ لَكُمۡ فِيهَا خَيۡرٞۖ فَٱذۡكُرُواْ ٱسۡمَ ٱللَّهِ عَلَيۡهَا صَوَآفَّۖ فَإِذَا وَجَبَتۡ جُنُوبُهَا فَكُلُواْ مِنۡهَا وَأَطۡعِمُواْ ٱلۡقَانِعَ وَٱلۡمُعۡتَرَّۚ كَذَٰلِكَ سَخَّرۡنَٰهَا لَكُمۡ لَعَلَّكُمۡ تَشۡكُرُونَ ﴾
[الحج: 36]

Ndi nyama zina tidazipanga kukhala ngati zina mwa zizindikiro za Mulungu ndipo mwa izo muli zofunika kwambiri kwa inu. Motero tchulani dzina la Mulungu pa izo pamene muziika kuti ziperekedwe nsembe. Ndipo zikaphedwa, idyani nyama yake ndiponso mumudyetse wopempha ndi amene apempha mwamanyazi. Kotero Ife nyamazi tazipereka kwa inu kuti mukhale othokoza

❮ Previous Next ❯

ترجمة: والبدن جعلناها لكم من شعائر الله لكم فيها خير فاذكروا اسم الله, باللغة نيانجا

﴿والبدن جعلناها لكم من شعائر الله لكم فيها خير فاذكروا اسم الله﴾ [الحج: 36]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo ngamira (ng’ombe, mbuzi ndi mbelere) tadzichita kwa inu kuti zikhale mwa zizindikiro za chipembedzo cha Allah; m’zimenezo muli zabwino kwa inu; choncho litchuleni dzina la Allah pa izo pamene zikuima mondanda (uku mukuzizinga,) ndipo zikagwa cham’nthiti, idyani (nyama yake) ndikumdyetsa yemwe akungozungulirazungulira, wosapempha ndi wopempha yemwe. Momwemo tazigonjetsa kwa inu (pochita kuti zikugonjereni) kuti muthokoze
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek