×

Ndipo kuti iwo amene adapatsidwa nzeru azindikire kuti ichi ndi choonadi chochokera 22:54 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-hajj ⮕ (22:54) ayat 54 in Chichewa

22:54 Surah Al-hajj ayat 54 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-hajj ayat 54 - الحج - Page - Juz 17

﴿وَلِيَعۡلَمَ ٱلَّذِينَ أُوتُواْ ٱلۡعِلۡمَ أَنَّهُ ٱلۡحَقُّ مِن رَّبِّكَ فَيُؤۡمِنُواْ بِهِۦ فَتُخۡبِتَ لَهُۥ قُلُوبُهُمۡۗ وَإِنَّ ٱللَّهَ لَهَادِ ٱلَّذِينَ ءَامَنُوٓاْ إِلَىٰ صِرَٰطٖ مُّسۡتَقِيمٖ ﴾
[الحج: 54]

Ndipo kuti iwo amene adapatsidwa nzeru azindikire kuti ichi ndi choonadi chochokera kwa Ambuye wako ndipo ayenera kukhulupirira ndi kuti mitima yawo ikhale yodzichepetsa chifukwa cha iyo. Ndithudi Mulungu ndi Mtsogoleri wa iwo amene akhulupirira njira yoyenera

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وليعلم الذين أوتوا العلم أنه الحق من ربك فيؤمنوا به فتخبت له, باللغة نيانجا

﴿وليعلم الذين أوتوا العلم أنه الحق من ربك فيؤمنوا به فتخبت له﴾ [الحج: 54]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo kuti adziwe amene apatsidwa kuzindikira kuti chimenechi n’choonadi chochokera kwa Mbuye wako ndi kuchikhulupirira ndikuti mitima yawo idzichepetse kwa Iye; ndithu Allah ndi Woongolera ku njira yolunjika amene akhulupirira
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek