×

Ndipo anthu osakhulupirira adzapitirira kukayikira chivumbulutso mpaka pamene ora lomaliza lidzawapeza mwadzidzidzi 22:55 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-hajj ⮕ (22:55) ayat 55 in Chichewa

22:55 Surah Al-hajj ayat 55 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-hajj ayat 55 - الحج - Page - Juz 17

﴿وَلَا يَزَالُ ٱلَّذِينَ كَفَرُواْ فِي مِرۡيَةٖ مِّنۡهُ حَتَّىٰ تَأۡتِيَهُمُ ٱلسَّاعَةُ بَغۡتَةً أَوۡ يَأۡتِيَهُمۡ عَذَابُ يَوۡمٍ عَقِيمٍ ﴾
[الحج: 55]

Ndipo anthu osakhulupirira adzapitirira kukayikira chivumbulutso mpaka pamene ora lomaliza lidzawapeza mwadzidzidzi kapena mpaka pamene chilango cha tsiku louka kwa akufa chidzawadzera

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ولا يزال الذين كفروا في مرية منه حتى تأتيهم الساعة بغتة أو, باللغة نيانجا

﴿ولا يزال الذين كفروا في مرية منه حتى تأتيهم الساعة بغتة أو﴾ [الحج: 55]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo amene sadakhulupirire apitilira kukhala m’chikaiko ndi chimenecho (wadza nachocho) kufikira tsiku la chimaliziro liwadzera mowatutumutsa, kapena chiwadzera chilango pa tsiku lopanda chabwino (kwa iwo)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek