×

Kukadakhala kuti Mulungu sadaonetse chisomo ndi chifundo chake pa inu, m’moyo uno 24:14 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nur ⮕ (24:14) ayat 14 in Chichewa

24:14 Surah An-Nur ayat 14 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nur ayat 14 - النور - Page - Juz 18

﴿وَلَوۡلَا فَضۡلُ ٱللَّهِ عَلَيۡكُمۡ وَرَحۡمَتُهُۥ فِي ٱلدُّنۡيَا وَٱلۡأٓخِرَةِ لَمَسَّكُمۡ فِي مَآ أَفَضۡتُمۡ فِيهِ عَذَابٌ عَظِيمٌ ﴾
[النور: 14]

Kukadakhala kuti Mulungu sadaonetse chisomo ndi chifundo chake pa inu, m’moyo uno ndiponso m’moyo umene uli nkudza, mukadalangidwa kwambiri chifukwa cha zimene mwakhala mukuchita

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ولولا فضل الله عليكم ورحمته في الدنيا والآخرة لمسكم في ما أفضتم, باللغة نيانجا

﴿ولولا فضل الله عليكم ورحمته في الدنيا والآخرة لمسكم في ما أفضتم﴾ [النور: 14]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo pakadapanda ubwino wa Allah ndi chifundo Chake pa inu, pa dziko lapansi ndi patsiku la chimaliziro, chilango chachikulu chikadakukhudzani pa zomwe munkazijijirikira
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek