×

Iwo amene amasangalala kuti nkhani zoipa zokhudza anthu okhulupirira zifalikire, adzalangidwa kwambiri 24:19 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nur ⮕ (24:19) ayat 19 in Chichewa

24:19 Surah An-Nur ayat 19 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nur ayat 19 - النور - Page - Juz 18

﴿إِنَّ ٱلَّذِينَ يُحِبُّونَ أَن تَشِيعَ ٱلۡفَٰحِشَةُ فِي ٱلَّذِينَ ءَامَنُواْ لَهُمۡ عَذَابٌ أَلِيمٞ فِي ٱلدُّنۡيَا وَٱلۡأٓخِرَةِۚ وَٱللَّهُ يَعۡلَمُ وَأَنتُمۡ لَا تَعۡلَمُونَ ﴾
[النور: 19]

Iwo amene amasangalala kuti nkhani zoipa zokhudza anthu okhulupirira zifalikire, adzalangidwa kwambiri m’moyo umene uli nkudza. Mulungu ali kudziwa zonse pamene inu simudziwa

❮ Previous Next ❯

ترجمة: إن الذين يحبون أن تشيع الفاحشة في الذين آمنوا لهم عذاب أليم, باللغة نيانجا

﴿إن الذين يحبون أن تشيع الفاحشة في الذين آمنوا لهم عذاب أليم﴾ [النور: 19]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndithu amene akukonda kuti zoipa zifale pa amene akhulupirira, chilango chowawa chili pa iwo padziko lapansi ndi patsiku la chimaliziro. Ndipo Allah ndi yemwe akudziwa (zoyenerana ndi inu), koma inu simudziwa
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek