×

oh inu anthu okhulupirira m’choonadi! Musatsatire mapazi a Satana. Aliyense amene atsatira 24:21 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nur ⮕ (24:21) ayat 21 in Chichewa

24:21 Surah An-Nur ayat 21 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nur ayat 21 - النور - Page - Juz 18

﴿۞ يَٰٓأَيُّهَا ٱلَّذِينَ ءَامَنُواْ لَا تَتَّبِعُواْ خُطُوَٰتِ ٱلشَّيۡطَٰنِۚ وَمَن يَتَّبِعۡ خُطُوَٰتِ ٱلشَّيۡطَٰنِ فَإِنَّهُۥ يَأۡمُرُ بِٱلۡفَحۡشَآءِ وَٱلۡمُنكَرِۚ وَلَوۡلَا فَضۡلُ ٱللَّهِ عَلَيۡكُمۡ وَرَحۡمَتُهُۥ مَا زَكَىٰ مِنكُم مِّنۡ أَحَدٍ أَبَدٗا وَلَٰكِنَّ ٱللَّهَ يُزَكِّي مَن يَشَآءُۗ وَٱللَّهُ سَمِيعٌ عَلِيمٞ ﴾
[النور: 21]

oh inu anthu okhulupirira m’choonadi! Musatsatire mapazi a Satana. Aliyense amene atsatira mapazi a Satana, ndithudi, iye amalamulira zinthu zochititsa manyazi ndi zoipa. Koma pakadapanda chisomo cha Mulungu, panalibe wina wa inu amene akadayeretsedwa zoipa zake. Koma Mulungu amayeretsa aliyense amene Iye wamufuna. Mulungu amamva zonse ndiponso amadziwa chinthu china chilichonse

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ياأيها الذين آمنوا لا تتبعوا خطوات الشيطان ومن يتبع خطوات الشيطان فإنه, باللغة نيانجا

﴿ياأيها الذين آمنوا لا تتبعوا خطوات الشيطان ومن يتبع خطوات الشيطان فإنه﴾ [النور: 21]

Khaled Ibrahim Betala
“E inu amene mwakhulupiliira! Musatsatire mapazi a satana. Ndipo amene atsatire mapazi a satana (asokera) ndithudi iye akulamula zauve ndi zoipa. Ndipo pakadapanda ubwino wa Allah ndi chifundo Chake pa inu, sakadayera aliyense mwa inu mpaka kalekale. Koma Allah amamuyeretsa amene wamfuna. Ndipo Allah Ngwakumva zonse; Wodziwa kwambiri
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek