×

Musalole kuti anthu olemera ndi olemekezeka amene ali pakati panu kuti alumbire 24:22 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nur ⮕ (24:22) ayat 22 in Chichewa

24:22 Surah An-Nur ayat 22 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nur ayat 22 - النور - Page - Juz 18

﴿وَلَا يَأۡتَلِ أُوْلُواْ ٱلۡفَضۡلِ مِنكُمۡ وَٱلسَّعَةِ أَن يُؤۡتُوٓاْ أُوْلِي ٱلۡقُرۡبَىٰ وَٱلۡمَسَٰكِينَ وَٱلۡمُهَٰجِرِينَ فِي سَبِيلِ ٱللَّهِۖ وَلۡيَعۡفُواْ وَلۡيَصۡفَحُوٓاْۗ أَلَا تُحِبُّونَ أَن يَغۡفِرَ ٱللَّهُ لَكُمۡۚ وَٱللَّهُ غَفُورٞ رَّحِيمٌ ﴾
[النور: 22]

Musalole kuti anthu olemera ndi olemekezeka amene ali pakati panu kuti alumbire kuti sadzapereka chithandizo kwa abale awo, kwa anthu osauka ndiponso kwa iwo amene adathawa ku midzi yawo chifukwa cha nkhani zokhudza Mulungu. Iwo ayenera kuwakhululukira ndi kuwalekerera. Kodi inu simufuna kuti Mulungu akukhululukireni? Mulungu ndi Mwini chikhululukiro ndiponso Mwini chisoni chosatha

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ولا يأتل أولو الفضل منكم والسعة أن يؤتوا أولي القربى والمساكين والمهاجرين, باللغة نيانجا

﴿ولا يأتل أولو الفضل منكم والسعة أن يؤتوا أولي القربى والمساكين والمهاجرين﴾ [النور: 22]

❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek