×

Kodi inu simuona mmene Mulungu amayendetsera mitambo? Ndipo amaisonkhanitsira ndi kuiika m’gulu 24:43 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nur ⮕ (24:43) ayat 43 in Chichewa

24:43 Surah An-Nur ayat 43 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nur ayat 43 - النور - Page - Juz 18

﴿أَلَمۡ تَرَ أَنَّ ٱللَّهَ يُزۡجِي سَحَابٗا ثُمَّ يُؤَلِّفُ بَيۡنَهُۥ ثُمَّ يَجۡعَلُهُۥ رُكَامٗا فَتَرَى ٱلۡوَدۡقَ يَخۡرُجُ مِنۡ خِلَٰلِهِۦ وَيُنَزِّلُ مِنَ ٱلسَّمَآءِ مِن جِبَالٖ فِيهَا مِنۢ بَرَدٖ فَيُصِيبُ بِهِۦ مَن يَشَآءُ وَيَصۡرِفُهُۥ عَن مَّن يَشَآءُۖ يَكَادُ سَنَا بَرۡقِهِۦ يَذۡهَبُ بِٱلۡأَبۡصَٰرِ ﴾
[النور: 43]

Kodi inu simuona mmene Mulungu amayendetsera mitambo? Ndipo amaisonkhanitsira ndi kuiika m’gulu limodzi ndipo inu mumaona mvula ili kuchokera mu mitamboyo. Kuchokera ku mapiri a kumwamba, Iye amatumiza mphepo kuti ipeze kumupeza wina aliyense amene wamufuna ndi kusiya aliyense amene wamufuna. Chilangali cha mphenzi zake chimakhala pang’ono kuti chilande maso a anthu

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ألم تر أن الله يزجي سحابا ثم يؤلف بينه ثم يجعله ركاما, باللغة نيانجا

﴿ألم تر أن الله يزجي سحابا ثم يؤلف بينه ثم يجعله ركاما﴾ [النور: 43]

Khaled Ibrahim Betala
“Kodi suona kuti Allah akuyendetsa mitambo, kenako nkuikumanitsa pamodzi, ndipo kenako nkuikhazika m’milumilu? Nuona mvula ikutuluka pakati pa iyo. Iye akutsitsa mapiri amitambo kuchokera kumwamba momwe muli mvula yamatalala; ndipo amamenya nawo amene wamfuna, ndikumpewetsa amene wamfuna. Kung’anima kwake kumayandikira kuchititsa khungu
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek