×

Musamuitane Mtumwi pomutchula dzina monga momwe mumaitanirana wina ndi mnzake. Mulungu amadziwa 24:63 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nur ⮕ (24:63) ayat 63 in Chichewa

24:63 Surah An-Nur ayat 63 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nur ayat 63 - النور - Page - Juz 18

﴿لَّا تَجۡعَلُواْ دُعَآءَ ٱلرَّسُولِ بَيۡنَكُمۡ كَدُعَآءِ بَعۡضِكُم بَعۡضٗاۚ قَدۡ يَعۡلَمُ ٱللَّهُ ٱلَّذِينَ يَتَسَلَّلُونَ مِنكُمۡ لِوَاذٗاۚ فَلۡيَحۡذَرِ ٱلَّذِينَ يُخَالِفُونَ عَنۡ أَمۡرِهِۦٓ أَن تُصِيبَهُمۡ فِتۡنَةٌ أَوۡ يُصِيبَهُمۡ عَذَابٌ أَلِيمٌ ﴾
[النور: 63]

Musamuitane Mtumwi pomutchula dzina monga momwe mumaitanirana wina ndi mnzake. Mulungu amadziwa ena a inu amene amazemba ndi kuchoka pakati panu. Aleke onse amene samvera Mtumwi kuti achenjere mwina mayesero kapena chilango chowawa chikhoza kugwa pa iwo

❮ Previous Next ❯

ترجمة: لا تجعلوا دعاء الرسول بينكم كدعاء بعضكم بعضا قد يعلم الله الذين, باللغة نيانجا

﴿لا تجعلوا دعاء الرسول بينكم كدعاء بعضكم بعضا قد يعلم الله الذين﴾ [النور: 63]

Khaled Ibrahim Betala
“Kumuitana Mtumiki pakati panu musakuchite monga momwe mumaitanirana nokhanokha, ndithu Allah akudziwa amene akuchoka pamalo mozemba ndi modzibisa mwa inu. Choncho achenjere amene akunyozera lamulo lake kuti mliri ungawapeze, kapena kuwapeza chilango chowawa
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek