×

Ndipo kudzanenedwa kwa iwo kuti, “Itanani anzanu kuti akuthandizeni.” Iwo adzawaitana koma 28:64 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Qasas ⮕ (28:64) ayat 64 in Chichewa

28:64 Surah Al-Qasas ayat 64 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Qasas ayat 64 - القَصَص - Page - Juz 20

﴿وَقِيلَ ٱدۡعُواْ شُرَكَآءَكُمۡ فَدَعَوۡهُمۡ فَلَمۡ يَسۡتَجِيبُواْ لَهُمۡ وَرَأَوُاْ ٱلۡعَذَابَۚ لَوۡ أَنَّهُمۡ كَانُواْ يَهۡتَدُونَ ﴾
[القَصَص: 64]

Ndipo kudzanenedwa kwa iwo kuti, “Itanani anzanu kuti akuthandizeni.” Iwo adzawaitana koma iwo sadzawamva ayi. Ndipo iwo adzalawa chilango chowawa. Iwo adzafunitsitsa akadatsogozedwa bwino

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وقيل ادعوا شركاءكم فدعوهم فلم يستجيبوا لهم ورأوا العذاب لو أنهم كانوا, باللغة نيانجا

﴿وقيل ادعوا شركاءكم فدعوهم فلم يستجيبوا لهم ورأوا العذاب لو أنهم كانوا﴾ [القَصَص: 64]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo kudzanenedwa: “Itanani aphatikizi anu.” Choncho adzawaitana koma sadzawayankha. Ndipo azawawona mavuto (pa nthawiyo azakhumba) akadakhala oongoka (pa dziko lapansi kotero kuti akadapeza mtendere pa tsiku la chimaliziro)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek