×

Ndipo adamutola iye a banja la Farawo kuti akhoza kukhala mdani ndiponso 28:8 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Qasas ⮕ (28:8) ayat 8 in Chichewa

28:8 Surah Al-Qasas ayat 8 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Qasas ayat 8 - القَصَص - Page - Juz 20

﴿فَٱلۡتَقَطَهُۥٓ ءَالُ فِرۡعَوۡنَ لِيَكُونَ لَهُمۡ عَدُوّٗا وَحَزَنًاۗ إِنَّ فِرۡعَوۡنَ وَهَٰمَٰنَ وَجُنُودَهُمَا كَانُواْ خَٰطِـِٔينَ ﴾
[القَصَص: 8]

Ndipo adamutola iye a banja la Farawo kuti akhoza kukhala mdani ndiponso madandaulo kwa iwo. Ndithudi Farawo, Hamani ndi Asirikali awo, onse adali ochimwa

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فالتقطه آل فرعون ليكون لهم عدوا وحزنا إن فرعون وهامان وجنودهما كانوا, باللغة نيانجا

﴿فالتقطه آل فرعون ليكون لهم عدوا وحزنا إن فرعون وهامان وجنودهما كانوا﴾ [القَصَص: 8]

Khaled Ibrahim Betala
“Choncho adamtola anthu a Farawo kuti mapeto ake adzakhale m’dani kwa iwo ndi odandaulitsa. Ndithu Farawo ndi Hamana ndi magulu awo ankhondo adali olakwa
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek