×

Mkazi wake wa Farawo adati kwa iye, “Mwana uyu akhoza kubweretsa chisangalalo 28:9 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Qasas ⮕ (28:9) ayat 9 in Chichewa

28:9 Surah Al-Qasas ayat 9 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Qasas ayat 9 - القَصَص - Page - Juz 20

﴿وَقَالَتِ ٱمۡرَأَتُ فِرۡعَوۡنَ قُرَّتُ عَيۡنٖ لِّي وَلَكَۖ لَا تَقۡتُلُوهُ عَسَىٰٓ أَن يَنفَعَنَآ أَوۡ نَتَّخِذَهُۥ وَلَدٗا وَهُمۡ لَا يَشۡعُرُونَ ﴾
[القَصَص: 9]

Mkazi wake wa Farawo adati kwa iye, “Mwana uyu akhoza kubweretsa chisangalalo kwa ine ndi iwe. Musamuphe ayi. Mwina akhoza kutithandiza kapena tikhoza kumutenga kuti akhale mwana wathu.” Koma iwo sadadziwe chimene anali kuchita

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وقالت امرأة فرعون قرة عين لي ولك لا تقتلوه عسى أن ينفعنا, باللغة نيانجا

﴿وقالت امرأة فرعون قرة عين لي ولك لا تقتلوه عسى أن ينفعنا﴾ [القَصَص: 9]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo mkazi wa Farawo adati: “(Musamuphe, akhale) chosangalatsa diso langa ndi lako; musamuphe mwina angatithandize, kapena tingam’chite kukhala mwana (wathu.” Adanena izi) iwo asakudziwa (kuti adzakhala m’dani wawo)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek