×

Patsiku limene nkhope zina zidzakhala zowala ndi za chimwemwe pamene zina zidzakhala 3:106 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:106) ayat 106 in Chichewa

3:106 Surah al-‘Imran ayat 106 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 106 - آل عِمران - Page - Juz 4

﴿يَوۡمَ تَبۡيَضُّ وُجُوهٞ وَتَسۡوَدُّ وُجُوهٞۚ فَأَمَّا ٱلَّذِينَ ٱسۡوَدَّتۡ وُجُوهُهُمۡ أَكَفَرۡتُم بَعۡدَ إِيمَٰنِكُمۡ فَذُوقُواْ ٱلۡعَذَابَ بِمَا كُنتُمۡ تَكۡفُرُونَ ﴾
[آل عِمران: 106]

Patsiku limene nkhope zina zidzakhala zowala ndi za chimwemwe pamene zina zidzakhala za kuda.Anthu amene adzakhala ndi nkhope zakuda adzafunsidwa kuti: “Kodi inu mudakana chikhulupiriro mutachivomera poyamba? Motero lawani chilango, chifukwa chokana kukhulupilira.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: يوم تبيض وجوه وتسود وجوه فأما الذين اسودت وجوههم أكفرتم بعد إيمانكم, باللغة نيانجا

﴿يوم تبيض وجوه وتسود وجوه فأما الذين اسودت وجوههم أكفرتم بعد إيمانكم﴾ [آل عِمران: 106]

Khaled Ibrahim Betala
“Patsikulo nkhope zina zidzakhala zowala pomwe nkhope zina zidzakhala zakuda. Tsono amene nkhope zawo zidzakhala zakuda, (adzauzidwa): “Kodi mudakana ( Allah) pambuyo pa chikhulupiliro chanu? Choncho, lawani chilango (chopweteka) chifukwa cha zomwe mudali kuzikana.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek